Nthawi Lyrics

M'dalitso wako udzatsika
Chisomo chake chidzatsika
Nthawi yako idzafika
Nyengo zako zidzasintha
Chilichonse chomwe udzagwire
Chidzabala zipatso, chidzabala zipatso
Thembelero lawo lidzakhala m'dalitso
Manyozo adzakhala matamando
Madando ako adzapeza mayankho
Nthawi, Nthawi idzafika
Nthawi idzafika, nthawi idzafika
Chimwemwe sindalama ai
Usauzunze mtima
Nthawi idzafika
Nthawi, Nthawi idzafika
Nthawi idzafika, nthawi idzafika
Chimwemwe sindalama ai
Usauzunze mtima
Nthawi idzafika
Kupambana kosatha
Mtendere uzadza
Mavuto adzatha, ingokhulupilira
Sudzasowa kanthu
Sudzanyozekanso
Sudzaderanso nkhawa
Chilichonse olo usanapemphe
Ambuye adzapatsa, Ambuye adzapatsa
Thembelero lawo lidzakhala m'dalitso
Manyozo adzakhala matamando
Madando ako adzapeza mayankho
Oh, oh
Nthawi, Nthawi idzafika
Nthawi idzafika, Nthawi idzafika
Chimwemwe sindalama ai
Usauzunze mtima
Nthawi idzafika
Nthawi, Nthawi idzafika
Nthawi idzafika, Nthawi idzafika
Chimwemwe sindalama ai
Usauzunze mtima
Nthawi idzafika
Zonse umakhumba, umafuna
Osakakamiza...
Nthawi, Nthawi nthawi
WATCH VIDEO
ABOUT THIS SONG
Release Year : 2021
Album : Nthawi (Single)
Copyright : (c) 2021
Added By : Huntyr Kelx
SEE ALSO
AUTHOR
YOU MAY ALSO LIKE