Home Search Countries Albums

Compensation

DRIEMO

Compensation Lyrics


Kuti mwina compensation
Driemo
Ndidzapereke moyo wanga

Oh mtima uwupereke, kwaine ndiwutenge
Don't you worry about safety
Ndidzachengetera chengetera chengetera
I know mtima unaswekapo
You've been there unalirapo, ululu mumtima kufikapo
Ukaganizira ganizira ganizira
Paiwe ndilola ndipepere, chikondi chisaperewere
Olo pa ground paterere I will love you the same baby

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Don't be scared to love me more
Zakale zapita it's me and you
Undiuze pomwe Pali mantha ako
I know mtima umakana ukandiunika
Umaona ngati Aja anakunamiza koma
I wanna be your soldier
Your fighter
Protector
Defender
I just wanna be your friend for life

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Ooh udzandifunse
Udzandifunse, mwina compensation ndidzapereke moyo wanga eeee

Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga
Oh udzandifunse
Ndikadzakuswera mtima udzandifunse
Kuti mwina compensation
Ndidzapereke moyo wanga

Enjoy Synced Lyrics With Our Mobile App

Download on Google PlayGet it on App Store

WATCH VIDEO

ABOUT THIS SONG


Release Year : 2022


Album : Compensation (Single)


Added By : Farida

SEE ALSO

AUTHOR

DRIEMO

Malawi

Driemo is a Malawian Afro pop Artist ...

YOU MAY ALSO LIKE